Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 23:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo adzakudzera ndi zida, magareta a nkhondo, ndi magareta ena, pamodzi ndi msonkhano wa mitundu ya anthu; adzadziikira pozungulira pako ndi zikopa zocinjiriza ndi zisoti; ndipo ndidzawaika aweruze, nadzakuweruza monga mwa maweruzo ao.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 23

Onani Ezekieli 23:24 nkhani