Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 9:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Popeza ife ndife akapolo, koma Mulungu wathu sanatisiya m'ukapolo wathu, natifikitsira cifundo pamaso pa mafumu a Perisiya, kuti atitsitsimutse kuimika nyumba ya Mulungu wathu, ndi kukonzanso muunda wace, ndi kutipatsa linga m'Yuda ndi m'Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu Ezara 9

Onani Ezara 9:9 nkhani