Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 9:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ciyambire masiku a makolo athu taparamula kwakukuru mpaka lero lino; ndi cifukwa ca mphulupulu zathu ife, mafumu athu, ndi ansembe athu, tinaperekedwa m'dzanja la mafumu a maikowo, kulupanga kundende, ndi kufunkhidwa, ndi kucitidwa manyazi pankhope pathu, monga lero lino.

Werengani mutu wathunthu Ezara 9

Onani Ezara 9:7 nkhani