Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 9:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

kodi tidzabwereza kuphwanya malamulo anu, ndi kukwatana nayo mitundu ya anthu ocita zonyansa izi? Simudzakwiya nafe kodi mpaka mwatitha, ndi kuti pasakhale otsala kapena akupulumuka?

Werengani mutu wathunthu Ezara 9

Onani Ezara 9:14 nkhani