Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 7:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pamodzi ndi siliva ndi golidi ziri zonse ukazipeza m'dziko lonse la ku Babulo, pamodzi ndi copereka caufulu ca anthu, ndi ca ansembe, akuperekera mwaufulu nyumba ya Mulungu wao iri ku Yerusalemu;

Werengani mutu wathunthu Ezara 7

Onani Ezara 7:16 nkhani