Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 4:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Zerubabele, ndi Yesuwa, ndi akuru otsala a nyumba za makolo a Israyeli, anati kwa iwo, Sikuyenera ndi inu ndi ife kumangira Mulungu wathu nyumba, koma ife tokha pamodzi tidzamangira Yehova Mulungu wa Israyeli, monga mfumu Koresi mfumu ya Perisiya watilamulira.

Werengani mutu wathunthu Ezara 4

Onani Ezara 4:3 nkhani