Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 10:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo Sekaniya mwana wa Yehiyeli, mwana wina wa Elamu, anambwezera Ezara mau, nati, Talakwira Mulungu wathu, tadzitengera akazi acilendo a mitundu ya dzikoli; koma tsopano cimtsalira Israyeli ciyembekezo kunena za cinthu ici.

Werengani mutu wathunthu Ezara 10

Onani Ezara 10:2 nkhani