Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 10:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsono tipangane ndi Mulungu wathu kucotsa akazi onse, ndi obadwa mwa iwo, monga mwa uphungu wa mbuye wanga, ndi wa iwo akunjenjemera pa lamulo la Mulungu wathu; ndipo cicitike monga mwa cilamulo.

Werengani mutu wathunthu Ezara 10

Onani Ezara 10:3 nkhani