Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 35:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anadza, ali yense wofulumidwa mtima, ndi yense mzimu wace wamfunitsa, nabwera naco copereka ca Yehova, ca ku nchito ya cihema cokomanako, ndi ku utumiki wace wonse, ndi ku zobvala zopatulika.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 35

Onani Eksodo 35:21 nkhani