Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 18:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo iwo aweruze mirandu ya anthu nthawi zonse; ndipo kudzakhala kuti mirandu yaikuru yonse abwere nayo kwa iwe; koma mirandu yaing'ono yonse aweruze okha; potero idzakucepera nchito, ndi iwo adzasenza nawe.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 18

Onani Eksodo 18:22 nkhani