Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 18:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene mpongozi wace wa Mose anaona zonsezi iye anawacitira anthu, anati, Cinthu ici nciani uwacitira anthuci? Umakhala pa wekha bwanji, ndi anthu onse amakhala ciriri pamaso pako kuyambira m'mawa kufikira madzulo?

Werengani mutu wathunthu Eksodo 18

Onani Eksodo 18:14 nkhani