Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 18:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunatero kuti m'mawa mwace Mose anakhala pansi kuweruzira anthu mirandu yao; ndipo anthu anakhala ciriri pamaso pa Mose kuyambira m'mawa kufikira madzulo.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 18

Onani Eksodo 18:13 nkhani