Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 12:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cisapezeke cotupitsa m'nyumba zanu masiku asanu ndi awiri; pakuti ali yense wakudya kanthu ka cotupitsa, munthuyo adzasadzidwa ku msonkhano wa Israyeli, angakhale ndiye mlendo kapena wobadwa m'dziko.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 12

Onani Eksodo 12:19 nkhani