Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 8:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mukumbukile njira yonse imene Yehova Mulungu wanu anakuyendetsani m'cipululu zaka izi makumi anai, kuti akucepetseni, kukuyesani, kudziwa cokhala mumtima mwanu, ngati mudzasunga malamulo ace, kapena iai.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 8

Onani Deuteronomo 8:2 nkhani