Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 8:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Muzisamalira kucita malamulo onse amene ndikuuzani lero lino, kuti mukhale ndi moyo, ndi kucuruka, ndi kulowa, ndi kulandira dziko limene Yehova analumbirira makolo anu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 8

Onani Deuteronomo 8:1 nkhani