Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 7:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mafano osema a milungu yao muwateothe ndi moto; musamasirira siliva ndi golidi ziri pa iwo, kapena kudzitengera izi; mungakodwe nazo; pakuti izi zinyansira Yehova Mulungu wanu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 7

Onani Deuteronomo 7:25 nkhani