Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 7:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mudzakhala odalitsika koposa mitundu yonse ya anthu; sipadzakhala mwamuna kapena wamkazi wosabala pakati pa inu, kapena pakati pa zoweta zanu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 7

Onani Deuteronomo 7:14 nkhani