17. Usaphe.
18. Usacite cigololo.
19. Usabe.
20. Usamnamizire mnzako.
21. Usasirire mkazi wace wa mnzako; usakhumbe nyumba yace ya mnzako, munda wace, kapena wanchito wace wamwamuna, kapena wanchito wace wamkazi, ng'ombe yace, kapena buru wace, kapena kanthu kali konse ka mnzako.