Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 28:65 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mwa a mitundu iyi simudzapumula, inde sipadzakhala popumulira phazi lanu; koma Yehova adzakupatsani kumeneko mtima wonjenjemera, m'maso mwanu mudzada, mudzafa ndi kulefuka mtima.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 28

Onani Deuteronomo 28:65 nkhani