Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 28:64 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova adzakubalalitsani mwa mitundu yonse ya anthu, kuyambira malekezero a dziko lapansi kufikira malekezero a dziko lapansi; ndipo kumeneko mudzatumikira milungu yina, imene simunaidziwa, inu ndi makolo anu, yamitengo ndi yamiyala.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 28

Onani Deuteronomo 28:64 nkhani