Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 28:63 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kudzali kuti, monga Yehova anakondwera nanu kukucitirani zabwino, ndi kukucurukitsani; momwemo Yehova adzakondwera nanu kutayikitsa ndi kuononga inu, ndipo adzakuzulani kudziko kumene mulowako kulilandira.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 28

Onani Deuteronomo 28:63 nkhani