Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 23:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

popeza sanakukumikani ndi mkate ndi madzi m'njira muja munaturuka m'Aigupto; popezanso anakulembererani Balamu mwana wa Beori wa ku Petori wa Mesapotamiya, kuti akutemberereni.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 23

Onani Deuteronomo 23:4 nkhani