Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 15:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Zazimuna zonse zoyamba kubadwa, zobadwa mwa ng'ombe zanu ndi mwa nkhosa ndi mbuzi zanu, muzizipatulira Yehova Mulungu wanu; musamagwiritsa nchito yoyamba kubadwa mwa ng'ombe zanu, kapena kusenga yoyamba kubadwa ya nkhosa kapena mbuzi zanu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 15

Onani Deuteronomo 15:19 nkhani