Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 12:28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Samalirani ndi kumvera mau awa onse ndikuuzaniwa, kuti cikukomereni inu, ndi ana anu akudza m'mbuyo mwanu nthawi zonse, pocita inu zokoma ndi zoyenera pamaso pa Yehova Mulungu wanu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 12

Onani Deuteronomo 12:28 nkhani