Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 12:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo mupereke nsembe zanu zopsereza, nyama zao ndi mwazi wao, pa guwa la nsembe la Yehova Mulungu wanu; ndipo athire mwazi wa nsembe zanu zophera pa guwa la nsembe la Yehova Mulungu wanu, koma nyama yace muidye.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 12

Onani Deuteronomo 12:27 nkhani