Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 4:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nthawi yomweyo anacitika mau awa kwa Nebukadinezara; anamuinga kumcotsa kwa anthu; nadya udzu ngati ng'ombe iye, ndi thupi lace linakhathamira ndi mame a kumwamba, mpaka tsitsi lace lidamera ngati nthenga za ciombankhanga ndi makadabo ace ngati makadabo a mbalame.

Werengani mutu wathunthu Danieli 4

Onani Danieli 4:33 nkhani