Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 5:15-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

15. ndi Ibara ndi Elisua, ndi Nefegi ndi Yafiya;

16. ndi Elisama ndi Eliada ndi Elifeleti.

17. Koma pamene Afilisti anamva kuti adamdzoza Davide mfumu ya Israyeli, Afilisti onse anakwera kukafuna Davide; ndipo Davide anacimva natsikira kungaka kuja.

18. Tsono Afilisti anafika natanda m'cigwa ca Refaimu.

19. Ndipo Davide anafunsira kwa Yehova nati, Kodi ndimuke kuyambana nao Afilistiwo? Mudzawapereka m'dzanja langa kodi? Ndipo Yehova ananena ndi Davide, Pita, pakuti zoonadi ndidzapereka Afilisti m'dzanja lako.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 5