Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 5:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide anafunsira kwa Yehova nati, Kodi ndimuke kuyambana nao Afilistiwo? Mudzawapereka m'dzanja langa kodi? Ndipo Yehova ananena ndi Davide, Pita, pakuti zoonadi ndidzapereka Afilisti m'dzanja lako.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 5

Onani 2 Samueli 5:19 nkhani