Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 3:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsono pofika Yoabu ndi khamu lonse anali nalo, ena anamfotokozera Yoabu nati, Abineri mwana wa Neri anabwera kwa mfumu, amene analawirana naye, namuka iye mumtendereo

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 3

Onani 2 Samueli 3:23 nkhani