Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 20:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yoabu ananena ndi Amasa, Uli bwino mbale wanga? Ndipo Yoabu anagwira ndebvu za Amasa ndi dzanja lace lamanja kuti ampsompsone.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 20

Onani 2 Samueli 20:9 nkhani