Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 2:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma iye anakana kupambuka; cifukwa cace Abineri anamkantha ndi khali la mkondo m'mimba mwace, ndi khalilo linaturuka kumbuyo kwace. Ndipo anagwako, nafera pomwepo, Ndipo onse akufika kumalo kumene Asaheli anagwa, namwalirapo, anaima pomwepo.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 2

Onani 2 Samueli 2:23 nkhani