Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 15:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Itai nayankha mfumu nuti, Pali Yehova, pali mbuye wanga mfumu, zoonadi apo padzakhala mbuye wanga mfumu, kapena mpa imfa kapena mpa moyo, pomwepo padzakhalanso mnyamata wanu.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 15

Onani 2 Samueli 15:21 nkhani