Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 12:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma tsopano wafa, ndidzasaliranjinso kudya? Kodi ndikhoza kumbweza? Ine ndidzamuka kuli iye, koma iye sadzabweranso kwa ine.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 12

Onani 2 Samueli 12:23 nkhani