Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 12:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati iye, Pamene mwanayo akali ndi moyo, ndinasala kudya ndi kulira, pakuti ndinati, Adziwa ndani kapena Yehova adzandicitira cifundo kuti mwanayo akhale ndi moyo.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 12

Onani 2 Samueli 12:22 nkhani