Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 11:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali pa madzulo Davide anauka pa kama wace nayenda pa tsindwi la nyumba ya mfumu. Ndipo iye ali patsindwipo anaona mkazi alinkusamba; ndi mkaziyo anali wocititsa kaso pomuyang'ana.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 11

Onani 2 Samueli 11:2 nkhani