Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 34:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anadza kwa Hilikiya wansembe wamkulu, napereka ndarama adabwera nazo ku nyumba ya Mulungu, zimene Alevi osunga pakhomo adasonkhanitsa kuzilandira ku dzanja la Manase ndi Efraimu, ndi kwa otsala onse a Israyeli, ndi kwa Yuda yense, ndi Benjamini, ndi kwa okhala m'Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 34

Onani 2 Mbiri 34:9 nkhani