Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 30:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anaphera Paskha tsiku lakhumi ndi cinai la mwezi waciwiri, ndipo ansembe ndi Alevi anacita manyazi, nadzipatula, nabwera nazo nsembe zopsereza ku nyumba ya Yehova.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 30

Onani 2 Mbiri 30:15 nkhani