Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 29:31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo Hezekiya anayankha, nati, Tsopano mwadzipatulira kwa Yehova, senderani, bwerani nazo nsembe zophera ndi nsembe zoyamika ku nyumba ya Yehova. Ndi msonkhano unabwera nazo nsembe zophera ndi nsembe zoyamika, ndi onse a mtima wofuna mwini anabwera nazo nsembe zopsereza.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 29

Onani 2 Mbiri 29:31 nkhani