Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 29:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ansembe analowa m'kati mwace mwa nyumba ya Yehova kuiyeretsa, naturutsira ku bwalo la nyumba ya Yehova zoipsa zonse anazipeza m'Kacisi wa Yehova. Nazilandira Alevi, kuziturutsira kunja ku mtsinje wa Kedroni.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 29

Onani 2 Mbiri 29:16 nkhani