Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 29:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anamemeza abale ao, nadzipatula, nalowa monga adawauza mfumu mwa mau a Yehova, kuyeretsa nyumba ya Yehova.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 29

Onani 2 Mbiri 29:15 nkhani