Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 2:11-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Ndipo Huramu mfumu ya Turo anayankha ndi kulembera, natumiza kalatayo kwa Solomo, ndi kuti, Powakonda anthu ace Yehova anakulongani mfumu yao.

12. Huramu anatinso, Alemekezedwe Yehova Mulungu wa Israyeli, amene analenga kumwamba ndi dziko lapansi, nampatsa mfumu Davide mwana waluso, wodziwa nzeru ndi waluntha, ammangire Yehova nyumba, ndiponso nyumba ya ufumu wace.

13. Ndipo tsono ndatumiza munthu waluso wokhala Ralo, luntha, Huramu Abi,

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 2