Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 9:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mlonda ali ciriri pacilindiro m'Yezreeli, naona gulu la Yehu lirinkudza, nati, Ndiona gulu. Nati Yoramu, Tenga wapakavalo, numtumize akomane nao, nanene, Mtendere kodi?

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 9

Onani 2 Mafumu 9:17 nkhani