Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 9:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anamuka wapakavalo kukomana naye, nati, Atero mfumu, Mtendere kodi? Nati Yehu, Ngwanji mtendere, tembenukira m'mbuyo mwanga. Ndi mlonda anawafotokozera kuti, Mthenga wawafika, koma wosabwera.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 9

Onani 2 Mafumu 9:18 nkhani