Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 19:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Natuma Eliyakimu woyang'anira nyumbayo, ndi Sebina mlembi, ndi akuru a ansembe opfundira ciguduli, kwa Yesaya mneneri mwana wa Amozi.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 19

Onani 2 Mafumu 19:2 nkhani