Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 19:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, atamva Hezekiya, anang'amba zobvala zace, napfundira ciguduli, nalowa m'nyumba ya Yehova.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 19

Onani 2 Mafumu 19:1 nkhani