Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 30:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene anatsika naye, onani, iwo anabalalika apo ponse, analinkudya, ndi kumwa, ndi kudyerera, cifukwa ca cofunkha zambiri anazitenga ku dziko la Afilisti, ndi ku dziko la Yuda.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 30

Onani 1 Samueli 30:16 nkhani