Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 3:4-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Pamenepo Yehova anaitana Samueli; ndipo iye anayankha kuti, Ndiri pano.

5. Ndipo anathamangira kwa Eli nati, Ndine, popeza mwandiitana ine. Ndipo iye anati, Sindinaitana, kagone. Napita iye, nagona,

6. Ndipo Yehova anabwereza kumuitana, ndi kuti, Samueli. Ndipo Samueli anauka, napita kwa Eli, nati, Ndine, pakuti mwandiitana ndithu. Koma iye anayankha, Sindinaitana, mwana wanga; kagone.

7. Koma Samueli sanadziwe Yehova, ndiponso mau a Yehova sanaululidwe kwa iye.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 3