Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 3:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anabwereza kumuitana Samueli nthawi yacitatu. Ndipo iye anauka napita kwa Eli, nati, Ndine, pakuti mwandiitana ndithu. Ndipo Eli anazindikira kuti ndiye Yehova amene analikuitana mwanayo.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 3

Onani 1 Samueli 3:8 nkhani