Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 28:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ananena naye, Makhalidwe ace ndi otani? nati iye, Nkhalamba irikukwera yobvala mwinjiro. Pamenepo Sauli anazindikira kuti ndi Samueli, naweramitsa nkhope yace pansi, namgwadira.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 28

Onani 1 Samueli 28:14 nkhani