Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 28:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Samueli ananena ndi Sauli, Wandibvutiranji kundikweretsa kuno? Sauli nayankha, Ndirikusautsika kwambiri, pakuti Afilisti aponyana nkhondo ndi ine, ndipo Mulungu anandicokera, osandiyankhanso, kapena ndi aneneri, kapena ndi maloto; cifukwa cace ndakuitanani, kuti mundidziwitse cimene ndiyenera kucita.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 28

Onani 1 Samueli 28:15 nkhani